Home
Categories
EXPLORE
True Crime
Comedy
Society & Culture
Business
Sports
TV & Film
Technology
About Us
Contact Us
Copyright
© 2024 PodJoint
00:00 / 00:00
Sign in

or

Don't have an account?
Sign up
Forgot password
https://is1-ssl.mzstatic.com/image/thumb/Podcasts125/v4/0a/c1/a9/0ac1a9e2-104d-767b-4fe0-f9c90f5eab22/mza_9124716935541807532.jpg/600x600bb.jpg
Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Thru the Bible Chichewa
261 episodes
2 days ago
Pologalamu ya Tisanthule Baibulo ndi gawo limodzi lautumiki, ophunzitsa Baibulo, otchedwa ulendo m??baibulo (Thru the Bible). Mndandanda wamapogalamuwu unakonzedwa ndi Dr. J. Vernon McGee ndipo unatanthauzidwa mu zilankhulo zoposa zana zimodzi (100). Zinakonzedwa kuti pologalamu imodzi idzikhala ya mphindi makumi atatu (30) ndipo kuti pomaliza zidzathe kuthandiza omvera kumvetsetsa Baibulo lonse. Ndipo pakali pano mapologalamu onsewa tawaika pamakina a Intaneti. Ndife oyamika kuti mwasankha kuphunzira zambiri zokhudza mau a Mulungu kudzera mmapologalamuwa. Tikukulimbikitsani kuti mudzimvera pologalamu imodzi patsiku kuyambira lolemba mpaka lachisanu. Ngati mungakwanitse kutsatira ndondomekoyi, pakutha kwa zaka zisanu mudzakhala kuti mwawerenga Baibulo lonse.
Show more...
Christianity
Religion & Spirituality
RSS
All content for Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa is the property of Thru the Bible Chichewa and is served directly from their servers with no modification, redirects, or rehosting. The podcast is not affiliated with or endorsed by Podjoint in any way.
Pologalamu ya Tisanthule Baibulo ndi gawo limodzi lautumiki, ophunzitsa Baibulo, otchedwa ulendo m??baibulo (Thru the Bible). Mndandanda wamapogalamuwu unakonzedwa ndi Dr. J. Vernon McGee ndipo unatanthauzidwa mu zilankhulo zoposa zana zimodzi (100). Zinakonzedwa kuti pologalamu imodzi idzikhala ya mphindi makumi atatu (30) ndipo kuti pomaliza zidzathe kuthandiza omvera kumvetsetsa Baibulo lonse. Ndipo pakali pano mapologalamu onsewa tawaika pamakina a Intaneti. Ndife oyamika kuti mwasankha kuphunzira zambiri zokhudza mau a Mulungu kudzera mmapologalamuwa. Tikukulimbikitsani kuti mudzimvera pologalamu imodzi patsiku kuyambira lolemba mpaka lachisanu. Ngati mungakwanitse kutsatira ndondomekoyi, pakutha kwa zaka zisanu mudzakhala kuti mwawerenga Baibulo lonse.
Show more...
Christianity
Religion & Spirituality
Episodes (20/261)
Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Miyambo ya Solomoni
2 days ago
26 minutes 22 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Yesu Kristu ndiye sukulu yophunzirako nzeru
5 days ago
26 minutes 20 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Kodi nzeru, nchiyani?
6 days ago
25 minutes 22 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Chenjezo ku tchimo la chiwerewere/chigololo
1 week ago
25 minutes 17 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Zinthu zisanu ndi ziwiri zomwe Mulungu amadananazo
1 week ago
26 minutes 49 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Chiyero cha ukwati
1 week ago
28 minutes 31 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Kupereka malangizo oonjezera kwa mnyamata
1 week ago
27 minutes 47 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Kupitiliza kupereka malangizo kwa mnyamata
1 week ago
26 minutes 18 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Malangizo ochenjeza mnyamata
2 weeks ago
26 minutes 15 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Adani a mnyamata
2 weeks ago
25 minutes 33 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Mnyamata ayenera kukhala ndi nzeru pamene akumana ndi zovuta
2 weeks ago
26 minutes 10 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Malangizo kwa mnyamata amene akuyamba moyo watsopano
2 weeks ago
26 minutes 53 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Kusanthula chiyambi cha buku la Miyambo
2 weeks ago
27 minutes 3 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Paulo ndiye chitsanzo cha m’sirikari wabwino wa Kristu
3 weeks ago
26 minutes 36 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Chitetezo cha mpingo ngati msirikari
3 weeks ago
27 minutes 10 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Mpingo ngati m’sirikari uyenera kudziwa m’dani wake
3 weeks ago
26 minutes 35 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Mpingo Uyenera Kudziwa Mdani wake
3 weeks ago
25 minutes 41 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Mpingo uyenera kukhala msirikari wabwino wa Kristu
3 weeks ago
27 minutes 43 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Mpingo ndiye msirikari
4 weeks ago
27 minutes 12 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Kupitiliza kuona zochitika ndi mpingo
4 weeks ago
25 minutes 30 seconds

Tisanthule Baibulo @ ttb.twr.org/chichewa
Pologalamu ya Tisanthule Baibulo ndi gawo limodzi lautumiki, ophunzitsa Baibulo, otchedwa ulendo m??baibulo (Thru the Bible). Mndandanda wamapogalamuwu unakonzedwa ndi Dr. J. Vernon McGee ndipo unatanthauzidwa mu zilankhulo zoposa zana zimodzi (100). Zinakonzedwa kuti pologalamu imodzi idzikhala ya mphindi makumi atatu (30) ndipo kuti pomaliza zidzathe kuthandiza omvera kumvetsetsa Baibulo lonse. Ndipo pakali pano mapologalamu onsewa tawaika pamakina a Intaneti. Ndife oyamika kuti mwasankha kuphunzira zambiri zokhudza mau a Mulungu kudzera mmapologalamuwa. Tikukulimbikitsani kuti mudzimvera pologalamu imodzi patsiku kuyambira lolemba mpaka lachisanu. Ngati mungakwanitse kutsatira ndondomekoyi, pakutha kwa zaka zisanu mudzakhala kuti mwawerenga Baibulo lonse.